1
LUKA 11:13
Buku Lopatulika
BLP-2018
Potero, ngati inu, okhala oipa, mudziwa kupatsa ana anu mphatso zabwino, koposa kotani nanga Atate wanu wa Kumwamba adzapatsa Mzimu Woyera kwa iwo akumpempha Iye?
Compare
Explore LUKA 11:13
2
LUKA 11:9
Ndipo Ine ndinena ndi inu, Pemphani, ndipo adzakupatsani; funani, ndipo mudzapeza; gogodani ndipo adzakutsegulirani.
Explore LUKA 11:9
3
LUKA 11:10
Pakuti yense wakupempha alandira; ndi wofunayo apeza; ndi iye amene agogoda adzamtsegulira.
Explore LUKA 11:10
4
LUKA 11:2
Ndipo anati kwa iwo, M'mene mupemphera nenani, Atate, Dzina lanu liyeretsedwa; Ufumu wanu udze
Explore LUKA 11:2
5
LUKA 11:4
Ndipo mutikhululukire ife machimo athu; pakuti ifenso tikhululukira munthu yense wa mangawa athu. Ndipo musatitengere ife kokatiyesa.
Explore LUKA 11:4
6
LUKA 11:3
tipatseni ife tsiku ndi tsiku chakudya cha patsiku.
Explore LUKA 11:3
7
LUKA 11:34
Nyali ya thupi ndiyo diso lako; pamene paliponse diso lako lili langwiro thupi lako lonse liunikidwanso monsemo; koma likakhala loipa, thupi lako lomwe lili la mdima wokhawokha.
Explore LUKA 11:34
8
LUKA 11:33
Palibe munthu, atayatsa nyali, aiika m'chipinda chapansi, kapena pansi pa mbiya, koma pa choikapo chake, kuti iwo akulowamo aone kuunika.
Explore LUKA 11:33
Home
Bible
Plans
Videos