GENESIS 3:6

GENESIS 3:6 BLPB2014

Ndipo pamene anaona mkaziyo kuti mtengo unali wabwino kudya, ndi kuti unali wokoma m'maso, mtengo wolakalakika wakupatsa nzeru, anatenga zipatso zake, nadya, napatsanso mwamuna wake amene ali naye, nadya iyenso.

Бясплатныя планы чытання і малітвы, звязаныя з GENESIS 3:6