1
Genesis 29:20
Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
Choncho Yakobo anagwira ntchito zaka zisanu ndi ziwiri chifukwa cha Rakele. Koma kwa iye zaka zonsezi zinakhala ngati masiku wochepa chifukwa anamukonda Rakele.
Параўнаць
Даследуйце Genesis 29:20
2
Genesis 29:31
Pamene Mulungu anaona kuti Yakobo sankamukonda Leya kwambiri, Iye analola kuti Leya uja akhale ndi ana, ndi kuti Rakele akhale wosabala.
Даследуйце Genesis 29:31
Стужка
Біблія
Пляны чытаньня
Відэа