1
YOHANE 20:21-22
Buku Lopatulika
Chifukwa chake Yesu anatinso kwa iwo, Mtendere ukhale ndi inu; monga Atate wandituma Ine, Inenso ndituma inu. Ndipo pamene anati ichi anawapumira, nanena nao, Landirani Mzimu Woyera.
قارن
اكتشف YOHANE 20:21-22
2
YOHANE 20:29
Yesu ananena kwa iye, Chifukwa wandiona Ine, wakhulupirira; odala iwo akukhulupirira, angakhale sanaone.
اكتشف YOHANE 20:29
3
YOHANE 20:27-28
Pomwepo ananena kwa Tomasi, Bwera nacho chala chako kuno, nuone manja anga, ndipo bwera nalo dzanja lako, nuliike kunthiti yanga, ndipo usakhale wosakhulupirira, koma wokhulupirira. Tomasi anayankha nati kwa Iye, Ambuye wanga, ndi Mulungu wanga.
اكتشف YOHANE 20:27-28
الصفحة الرئيسية
الكتاب المقدس
خطط
فيديو