شعار YouVersion
الكتاب المقدسخططفيديوهات
إحصل على التطبيق
مُحدد اللغة
رمز البحث

آيات مشهورة من الكتاب المقدس منYOHANE 17

1

YOHANE 17:17

Buku Lopatulika

BLP-2018

Patulani iwo m'choonadi; mau anu ndi choonadi.

قارن

اكتشف YOHANE 17:17

2

YOHANE 17:3

Buku Lopatulika

BLP-2018

Koma moyo wosatha ndi uwu, kuti akadziwe Inu Mulungu woona yekha, ndi Yesu Khristu amene munamtuma.

قارن

اكتشف YOHANE 17:3

3

YOHANE 17:20-21

Buku Lopatulika

BLP-2018

Koma sindipempherera iwo okha, komanso iwo akukhulupirira Ine chifukwa cha mau ao; kuti onse akakhale amodzi, monga Inu Atate mwa Ine, ndi Ine mwa Inu, kuti iwonso akakhale mwa Ife: kuti dziko lapansi likakhulupirire kuti Inu munandituma Ine.

قارن

اكتشف YOHANE 17:20-21

4

YOHANE 17:15

Buku Lopatulika

BLP-2018

Sindipempha kuti muwachotse iwo m'dziko lapansi, koma kuti muwasunge iwo kuletsa woipayo.

قارن

اكتشف YOHANE 17:15

5

YOHANE 17:22-23

Buku Lopatulika

BLP-2018

Ndipo ulemerero umene mwandipatsa Ine ndapatsa iwo; kuti akhale amodzi, monga Ife tili mmodzi; Ine mwa iwo, ndi Inu mwa Ine, kuti akhale angwiro mwa mmodzi; kuti dziko lapansi lizindikire kuti Inu munandituma Ine, nimunawakonda iwo, monga momwe munakonda Ine.

قارن

اكتشف YOHANE 17:22-23

خطط قرأة مجانية و مواضيع تعبدية ذات صلة بYOHANE 17

الإصحاح السابق
الإصحاح التالي
YouVersion

تشجع للبحث عن علاقة حميمة مع الله كل يوم.

خدمة

حول‌

مهن

التطوع

المفكّرة

صحافة

روابط مفيدة

مساعدة

تبرع

اصدارات الكتاب المقدس

الأناجيل المسموعة

لغات الكتاب المقدس

آية اليوم


خدمة رقمية ل

Life.Church
English (US)

©2025 Life.Church / YouVersion

سياسة الخصوصيةالشروط
برنامج الكشف عن نقاط الضعف
فيسبوكتويترالإنستجرامموقع يوتيوببينتيريست

الصفحة الرئيسية

الكتاب المقدس

خطط

فيديوهات