1
Gen. 5:24
Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa
Iyeyu adayanjana ndi Mulungu moyo wake wonse. Ndipo sadaonekenso, chifukwa choti Mulungu adamtenga.
አወዳድር
{{ጥቅስ}} ያስሱ
2
Gen. 5:22
Enoki adakhala ndi moyo zaka zina 300, akuyanjana ndi Mulungu. Adaberekanso ana ena aamuna ndi aakazi.
3
Gen. 5:1
Mndandanda wa mibadwo yochokera mwa Adamu udayenda motere: (Mulungu polenga Adamu, adampanga muchifaniziro chake.
4
Gen. 5:2
Adalenga mwamuna ndi mkazi, ndipo adaŵadalitsa, naŵatchula dzina loti Anthu.)
ቤት
መጽሐፍ ቅዱስ
እቅዶች
ቪዲዮዎች