1
Genesis 40:8
Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
Iwo anayankha, “Tonse awiri talota maloto, koma palibe wotitanthauzira malotowo.” Pamenepo Yosefe anawawuza kuti, “Ndi Mulungu yekha amene amapereka matanthauzo a maloto. Uzeni ine maloto anu.”
አወዳድር
{{ጥቅስ}} ያስሱ
2
Genesis 40:23
Koma mkulu wa operekera zakumwa uja sanamukumbukire Yosefe ndipo anamuyiwaliratu.
ቤት
መጽሐፍ ቅዱስ
እቅዶች
ቪዲዮዎች