1
Genesis 38:10
Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
Zimene ankachitazi zinayipira Yehova. Choncho anamulanganso ndi imfa.
አወዳድር
{{ጥቅስ}} ያስሱ
2
Genesis 38:9
Koma Onani anadziwa kuti mwanayo sadzakhala wake. Choncho nthawi zonse pamene amagona naye mkaziyo, ankatayira umuna pansi kuti asamuberekere mwana mʼbale wake.
ቤት
መጽሐፍ ቅዱስ
እቅዶች
ቪዲዮዎች